Thu Apr 18 2024 11:50:18 GMT+0200 (South Africa Standard Time)

This commit is contained in:
Timothy Muzgatama 2024-04-18 11:50:19 +02:00
parent 996e9f632c
commit faa4d5976d
5 changed files with 5 additions and 2 deletions

View File

@ -1 +1 @@
+ Koma khamu lankhondolo linawononga midzi yonse yozungulira Gerari, + pakuti kuopa + Yehova kunagwera okhalamo. Ankhondo anafunkha midzi yonse, ndipo munali zofunkha zambiri mmenemo. Ankhondowo anawononga mahema a oŵeta ngombe; + Anatenga nkhosa + zambirimbiri ndi ngamila, kenako anabwerera ku Yerusalemu.
\v 14 Koma khamu lankhondolo linawononga midzi yonse yozungulira Gerari, pakuti kuopa Yehova kunagwera okhalamo. Ankhondo anafunkha midzi yonse, ndipo munali zofunkha zambiri mmenemo. \v 15 Ankhondowo anawononga mahema a oŵeta ngombe; Anatenga nkhosa zambirimbiri ndi ngamila, kenako anabwerera ku Yerusalemu.

1
15/01.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\c 15 \v 1 Mzimu wa Mulungu unadza pa Azariya mwana wa Odedi. \v 2 Anatuluka kukakumana ndi Asa nkumuuza kuti: “Ndimvereni, Asa, ndi Ayuda onse ndi Benjamini: Yehova ali nanu pamene inu muli ndi iye. Musiyeni, adzakusiyani.

1
15/03.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 3 \v 5 Tsopano kwa nthawi yaitali, Israyeli analibe Mulungu woona, wopanda wansembe wophunzitsa, ndiponso wopanda chilamulo. \v 4 Koma mmasautso awo anatembenukira kwa Yehova Mulungu wa Isiraeli ndi kumufunafuna, ndipo anamupeza. Mmasiku amenewo munalibe mtendere kwa iye wotuluka kapena amene ankalowa, chifukwa panali chipwirikiti chachikulu pa anthu onse okhala mdzikolo.

1
15/title.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
Mutu 15

View File

@ -161,9 +161,9 @@
"14-07",
"14-09",
"14-12",
"14-14",
"15-title",
"15-01",
"15-03",
"15-06",
"15-08",
"15-10",