Thu Apr 18 2024 11:50:18 GMT+0200 (South Africa Standard Time)
This commit is contained in:
parent
996e9f632c
commit
faa4d5976d
|
@ -1 +1 @@
|
|||
+ Koma khamu lankhondolo linawononga midzi yonse yozungulira Gerari, + pakuti kuopa + Yehova kunagwera okhalamo. Ankhondo anafunkha midzi yonse, ndipo munali zofunkha zambiri mmenemo. Ankhondowo anawononga mahema a oŵeta ng’ombe; + Anatenga nkhosa + zambirimbiri ndi ngamila, kenako anabwerera ku Yerusalemu.
|
||||
\v 14 Koma khamu lankhondolo linawononga midzi yonse yozungulira Gerari, pakuti kuopa Yehova kunagwera okhalamo. Ankhondo anafunkha midzi yonse, ndipo munali zofunkha zambiri mmenemo. \v 15 Ankhondowo anawononga mahema a oŵeta ng’ombe; Anatenga nkhosa zambirimbiri ndi ngamila, kenako anabwerera ku Yerusalemu.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\c 15 \v 1 Mzimu wa Mulungu unadza pa Azariya mwana wa Odedi. \v 2 Anatuluka kukakumana ndi Asa n’kumuuza kuti: “Ndimvereni, Asa, ndi Ayuda onse ndi Benjamini: Yehova ali nanu pamene inu muli ndi iye. Musiyeni, adzakusiyani.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 3 \v 5 Tsopano kwa nthawi yaitali, Israyeli analibe Mulungu woona, wopanda wansembe wophunzitsa, ndiponso wopanda chilamulo. \v 4 Koma m’masautso awo anatembenukira kwa Yehova Mulungu wa Isiraeli ndi kumufunafuna, ndipo anamupeza. M’masiku amenewo munalibe mtendere kwa iye wotuluka kapena amene ankalowa, chifukwa panali chipwirikiti chachikulu pa anthu onse okhala m’dzikolo.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
Mutu 15
|
|
@ -161,9 +161,9 @@
|
|||
"14-07",
|
||||
"14-09",
|
||||
"14-12",
|
||||
"14-14",
|
||||
"15-title",
|
||||
"15-01",
|
||||
"15-03",
|
||||
"15-06",
|
||||
"15-08",
|
||||
"15-10",
|
||||
|
|
Loading…
Reference in New Issue