1 line
313 B
Plaintext
1 line
313 B
Plaintext
\v 14 Koma khamu lankhondolo linawononga midzi yonse yozungulira Gerari, pakuti kuopa Yehova kunagwera okhalamo. Ankhondo anafunkha midzi yonse, ndipo munali zofunkha zambiri mmenemo. \v 15 Ankhondowo anawononga mahema a oŵeta ng’ombe; Anatenga nkhosa zambirimbiri ndi ngamila, kenako anabwerera ku Yerusalemu. |