1 line
386 B
Plaintext
1 line
386 B
Plaintext
\v 3 \v 5 Tsopano kwa nthawi yaitali, Israyeli analibe Mulungu woona, wopanda wansembe wophunzitsa, ndiponso wopanda chilamulo. \v 4 Koma m’masautso awo anatembenukira kwa Yehova Mulungu wa Isiraeli ndi kumufunafuna, ndipo anamupeza. M’masiku amenewo munalibe mtendere kwa iye wotuluka kapena amene ankalowa, chifukwa panali chipwirikiti chachikulu pa anthu onse okhala m’dzikolo. |