Thu Apr 18 2024 12:04:21 GMT+0200 (South Africa Standard Time)
This commit is contained in:
parent
a181a7f94f
commit
8e497b425e
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 9 Pakuti maso a Yehova ayang’ana pa dziko lonse lapansi, kuti adzionetsere wamphamvu kwa iwo amene mtima wawo uli wangwiro ndi Iye. Koma mwachita zopusa pankhaniyi. Kuyambira tsopano udzachita nkhondo.” \v 10 Pamenepo Asa anakwiyira wamasomphenyayo, ndipo anamuika m’ndende, pakuti anamukwiyira kwambiri pa nkhani imeneyi.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 11 Taonani, machitidwe a Asa, kuyambira pachiyambi mpaka kumapeto, taonani, zalembedwa m'buku la mafumu a Yuda ndi Israeli. \v 12 M’chaka cha 39 cha ulamuliro wake, Asa anadwala matenda a mapazi ake. Ngakhale kuti matenda ake anali aakulu kwambiri, iye sanapemphe thandizo kwa Yehova, koma kwa ochiritsa okha.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 13 Choncho Asa anagona pamodzi ndi makolo ake, ndipo anamwalira m’chaka cha 41 cha ufumu wake. \v 14 Iwo anamuika m’manda ake amene anadzikwirira mu Mzinda wa Davide. Anamugoneka pa chithatha chodzaza ndi fungo labwino ndi zonunkhira zosiyanasiyana zokonzedwa ndi odziwa kununkhira. Kenako anasonkha moto waukulu kwambiri pomulemekeza.
|
Loading…
Reference in New Issue