1 line
342 B
Plaintext
1 line
342 B
Plaintext
\v 13 Choncho Asa anagona pamodzi ndi makolo ake, ndipo anamwalira m’chaka cha 41 cha ufumu wake. \v 14 Iwo anamuika m’manda ake amene anadzikwirira mu Mzinda wa Davide. Anamugoneka pa chithatha chodzaza ndi fungo labwino ndi zonunkhira zosiyanasiyana zokonzedwa ndi odziwa kununkhira. Kenako anasonkha moto waukulu kwambiri pomulemekeza. |