1 line
314 B
Plaintext
1 line
314 B
Plaintext
\v 11 Taonani, machitidwe a Asa, kuyambira pachiyambi mpaka kumapeto, taonani, zalembedwa m'buku la mafumu a Yuda ndi Israeli. \v 12 M’chaka cha 39 cha ulamuliro wake, Asa anadwala matenda a mapazi ake. Ngakhale kuti matenda ake anali aakulu kwambiri, iye sanapemphe thandizo kwa Yehova, koma kwa ochiritsa okha. |