Thu Apr 18 2024 12:02:21 GMT+0200 (South Africa Standard Time)

This commit is contained in:
Timothy Muzgatama 2024-04-18 12:02:22 +02:00
parent 60462de10b
commit a181a7f94f
3 changed files with 3 additions and 1 deletions

View File

@ -1 +1 @@
\v 4 \v 5 Beni-hadadi anamvera Mfumu Asa ndipo anatumiza akuluakulu a asilikali ake kukamenyana ndi mizinda ya Isiraeli. Anakantha Ijoni, Dani, Abele Maimu , ndi midzi yonse yosungiramo zinthu ya Nafitali. Ndiyeno Basa atamva zimenezi, anasiya kumanga mzinda wa Rama nkuimitsa ntchito yake. \v 6 Kenako mfumu Asa anatenga Ayuda onse pamodzi naye. Anatenga miyala ndi matabwa a ku Rama, zimene Basa ankamangira mzindawo. Kenako Mfumu Asa anagwiritsa ntchito zomangirazo pomanga Geba ndi Mizipa.
\v 4 Beni-hadadi anamvera Mfumu Asa ndipo anatumiza akuluakulu a asilikali ake kukamenyana ndi mizinda ya Isiraeli. Anakantha Ijoni, Dani, Abele Maimu , ndi midzi yonse yosungiramo zinthu ya Nafitali. \v 5 Ndiyeno Basa atamva zimenezi, anasiya kumanga mzinda wa Rama nkuimitsa ntchito yake. \v 6 Kenako mfumu Asa anatenga Ayuda onse pamodzi naye. Anatenga miyala ndi matabwa a ku Rama, zimene Basa ankamangira mzindawo. Kenako Mfumu Asa anagwiritsa ntchito zomangirazo pomanga Geba ndi Mizipa.

1
16/07.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 7 Nthawi imeneyo Hanani wamasomphenya anapita kwa Asa mfumu ya Yuda, nati kwa iye, “Popeza wadalira mfumu ya Aramu, osadalira Yehova Mulungu wako. Mdzanja lanu, \v 8 Aakusi ndi Alibia sanali gulu lalikulu lankhondo, ndi magaleta ankhondo ndi apakavalo ambiri, koma popeza munadalira Yehova, iye anakupulumutsani.

View File

@ -175,6 +175,7 @@
"16-title",
"16-01",
"16-02",
"16-04",
"16-07",
"16-09",
"16-11",