Thu Apr 18 2024 12:02:21 GMT+0200 (South Africa Standard Time)
This commit is contained in:
parent
60462de10b
commit
a181a7f94f
|
@ -1 +1 @@
|
|||
\v 4 \v 5 Beni-hadadi anamvera Mfumu Asa ndipo anatumiza akuluakulu a asilikali ake kukamenyana ndi mizinda ya Isiraeli. Anakantha Ijoni, Dani, Abele Maimu , ndi midzi yonse yosungiramo zinthu ya Nafitali. Ndiyeno Basa atamva zimenezi, anasiya kumanga mzinda wa Rama n’kuimitsa ntchito yake. \v 6 Kenako mfumu Asa anatenga Ayuda onse pamodzi naye. Anatenga miyala ndi matabwa a ku Rama, zimene Basa ankamangira mzindawo. Kenako Mfumu Asa anagwiritsa ntchito zomangirazo pomanga Geba ndi Mizipa.
|
||||
\v 4 Beni-hadadi anamvera Mfumu Asa ndipo anatumiza akuluakulu a asilikali ake kukamenyana ndi mizinda ya Isiraeli. Anakantha Ijoni, Dani, Abele Maimu , ndi midzi yonse yosungiramo zinthu ya Nafitali. \v 5 Ndiyeno Basa atamva zimenezi, anasiya kumanga mzinda wa Rama n’kuimitsa ntchito yake. \v 6 Kenako mfumu Asa anatenga Ayuda onse pamodzi naye. Anatenga miyala ndi matabwa a ku Rama, zimene Basa ankamangira mzindawo. Kenako Mfumu Asa anagwiritsa ntchito zomangirazo pomanga Geba ndi Mizipa.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 7 Nthawi imeneyo Hanani wamasomphenya anapita kwa Asa mfumu ya Yuda, nati kwa iye, “Popeza wadalira mfumu ya Aramu, osadalira Yehova Mulungu wako. M’dzanja lanu, \v 8 Aakusi ndi Alibia sanali gulu lalikulu lankhondo, ndi magaleta ankhondo ndi apakavalo ambiri, koma popeza munadalira Yehova, iye anakupulumutsani.
|
|
@ -175,6 +175,7 @@
|
|||
"16-title",
|
||||
"16-01",
|
||||
"16-02",
|
||||
"16-04",
|
||||
"16-07",
|
||||
"16-09",
|
||||
"16-11",
|
||||
|
|
Loading…
Reference in New Issue