Thu Apr 18 2024 12:00:20 GMT+0200 (South Africa Standard Time)
This commit is contained in:
parent
96c0b1d51c
commit
60462de10b
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\c 16 \v 1 M’chaka cha 36 cha ulamuliro wa Asa, Basa mfumu ya Isiraeli anaukira Yuda ndipo anamanga mzinda wa Rama, kuti asalole aliyense kutuluka kapena kulowa m’dziko la Asa mfumu ya Yuda.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 2 Pamenepo Asa anatulutsa siliva ndi golide m’zosungiramo za m’nyumba ya Yehova, ndi za m’nyumba ya mfumu, nazitumiza kwa Beni-hadadi mfumu ya Aramu, wakukhala ku Damasiko. Iye anati: \v 3 “Pakhale pangano pakati pa ine ndi iwe, monga linali pakati pa bambo anga ndi atate wako. Taonani, ndakutumizirani siliva ndi golide. ine ndekha."
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 4 \v 5 Beni-hadadi anamvera Mfumu Asa ndipo anatumiza akuluakulu a asilikali ake kukamenyana ndi mizinda ya Isiraeli. Anakantha Ijoni, Dani, Abele Maimu , ndi midzi yonse yosungiramo zinthu ya Nafitali. Ndiyeno Basa atamva zimenezi, anasiya kumanga mzinda wa Rama n’kuimitsa ntchito yake. \v 6 Kenako mfumu Asa anatenga Ayuda onse pamodzi naye. Anatenga miyala ndi matabwa a ku Rama, zimene Basa ankamangira mzindawo. Kenako Mfumu Asa anagwiritsa ntchito zomangirazo pomanga Geba ndi Mizipa.
|
|
@ -175,7 +175,6 @@
|
|||
"16-title",
|
||||
"16-01",
|
||||
"16-02",
|
||||
"16-04",
|
||||
"16-07",
|
||||
"16-09",
|
||||
"16-11",
|
||||
|
|
Loading…
Reference in New Issue