1 line
331 B
Plaintext
1 line
331 B
Plaintext
\v 9 Pakuti maso a Yehova ayang’ana pa dziko lonse lapansi, kuti adzionetsere wamphamvu kwa iwo amene mtima wawo uli wangwiro ndi Iye. Koma mwachita zopusa pankhaniyi. Kuyambira tsopano udzachita nkhondo.” \v 10 Pamenepo Asa anakwiyira wamasomphenyayo, ndipo anamuika m’ndende, pakuti anamukwiyira kwambiri pa nkhani imeneyi. |