Thu Apr 18 2024 12:10:00 GMT+0200 (South Africa Standard Time)
This commit is contained in:
parent
08265202db
commit
0f265421c5
|
@ -1 +1 @@
|
|||
\v 7 M’chaka chachitatu cha ulamuliro wake, anatumiza akalonga ake, Beni-Haili, Obadiya, Zekariya, Netaneli ndi Mikaya kuti akaphunzitse m’mizinda ya Yuda. \v 8 pamodzi ndi Alevi: Semaya, Netaniya, Zebadiya, Asaheli, Semiramoti, Yehonatani, Adoniya, Tobiya, ndi Tobi-Adoniya; ndi pamodzi nao panali Elisama ndi Yehoramu ansembe. \v 9 Anaphunzitsa m’Yuda, ali nalo buku la chilamulo cha Yehova; Iwo anayendayenda m’mizinda yonse ya Yuda ndi kuphunzitsa pakati pa anthu.
|
||||
\v 7 M’chaka chachitatu cha ulamuliro wake, anatumiza akalonga ake, Beni-Haili, Obadiya, Zekariya, Netaneli ndi Mikaya kuti akaphunzitse m’mizinda ya Yuda. \v 8 Pamodzi ndi Alevi: Semaya, Netaniya, Zebadiya, Asaheli, Semiramoti, Yehonatani, Adoniya, Tobiya, ndi Tobi-Adoniya; ndi pamodzi nao panali Elisama ndi Yehoramu ansembe. \v 9 Anaphunzitsa m’Yuda, ali nalo buku la chilamulo cha Yehova; Iwo anayendayenda m’mizinda yonse ya Yuda ndi kuphunzitsa pakati pa anthu.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 10 Mantha a Yehova anagwera maufumu onse a maiko ozungulira Yuda, kotero kuti sanachite nkhondo ndi Yehosafati. \v 11 Afilisti ena anapatsa Yehosafati mphatso, ndi siliva ngati msonkho. Aarabu anam’bweretseranso nkhosa, nkhosa 7,700, ndi mbuzi 7,700.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 12 Yehosafati anakhala wamphamvu kwambiri. Anamanga mipanda yolimba kwambiri ndi mizinda yosungirako zinthu m’Yuda. \v 13 Anali ndi katundu wambiri m’mizinda ya Yuda, ndi asilikali—ankhondo amphamvu—m’Yerusalemu.
|
|
@ -184,6 +184,7 @@
|
|||
"17-01",
|
||||
"17-03",
|
||||
"17-05",
|
||||
"17-07",
|
||||
"17-10",
|
||||
"17-12",
|
||||
"17-14",
|
||||
|
|
Loading…
Reference in New Issue