Thu Apr 18 2024 12:08:21 GMT+0200 (South Africa Standard Time)
This commit is contained in:
parent
e77ec573f1
commit
08265202db
|
@ -1 +1 @@
|
|||
\v 3 Yehova anali ndi Yehosafati chifukwa anayenda m’njira zoyambirira za Davide bambo ake, ndipo sanafunefune Abaala. [[V]] \v 4 M’malo mwake, anadalira Mulungu wa bambo ake, ndipo anayenda m’malamulo ake, osati mogwirizana ndi zochita za Isiraeli.
|
||||
\v 3 Yehova anali ndi Yehosafati chifukwa anayenda m’njira zoyambirira za Davide bambo ake, ndipo sanafunefune Abaala. [[Mabaibulo ena akale alibe "David" , choncho, matembenuzidwe ena amakono amasiya.]] \v 4 M’malo mwake, anadalira Mulungu wa bambo ake, ndipo anayenda m’malamulo ake, osati mogwirizana ndi zochita za Isiraeli.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 5 Momwemo Yehova anakhazikitsa lamulo m'dzanja lace; Ayuda onse anabweretsa mitulo kwa Yehosafati. Anali ndi chuma ndi ulemu wochuluka. \v 6 Mtima wake unali wodzipereka ku njira za Yehova. + Anachotsanso misanje ndi mizati ya Asera m’Yuda.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 7 M’chaka chachitatu cha ulamuliro wake, anatumiza akalonga ake, Beni-Haili, Obadiya, Zekariya, Netaneli ndi Mikaya kuti akaphunzitse m’mizinda ya Yuda. \v 8 pamodzi ndi Alevi: Semaya, Netaniya, Zebadiya, Asaheli, Semiramoti, Yehonatani, Adoniya, Tobiya, ndi Tobi-Adoniya; ndi pamodzi nao panali Elisama ndi Yehoramu ansembe. \v 9 Anaphunzitsa m’Yuda, ali nalo buku la chilamulo cha Yehova; Iwo anayendayenda m’mizinda yonse ya Yuda ndi kuphunzitsa pakati pa anthu.
|
|
@ -182,8 +182,8 @@
|
|||
"16-13",
|
||||
"17-title",
|
||||
"17-01",
|
||||
"17-03",
|
||||
"17-05",
|
||||
"17-07",
|
||||
"17-10",
|
||||
"17-12",
|
||||
"17-14",
|
||||
|
|
Loading…
Reference in New Issue