1 line
476 B
Plaintext
1 line
476 B
Plaintext
\v 7 M’chaka chachitatu cha ulamuliro wake, anatumiza akalonga ake, Beni-Haili, Obadiya, Zekariya, Netaneli ndi Mikaya kuti akaphunzitse m’mizinda ya Yuda. \v 8 Pamodzi ndi Alevi: Semaya, Netaniya, Zebadiya, Asaheli, Semiramoti, Yehonatani, Adoniya, Tobiya, ndi Tobi-Adoniya; ndi pamodzi nao panali Elisama ndi Yehoramu ansembe. \v 9 Anaphunzitsa m’Yuda, ali nalo buku la chilamulo cha Yehova; Iwo anayendayenda m’mizinda yonse ya Yuda ndi kuphunzitsa pakati pa anthu. |