Sat Apr 20 2024 10:04:18 GMT+0200 (South Africa Standard Time)

This commit is contained in:
Timothy Muzgatama 2024-04-20 10:04:20 +02:00
parent bfe3ff5f4e
commit ada4c38706
3 changed files with 3 additions and 1 deletions

View File

@ -1 +1 @@
Yehosafati anamanga zombo za ku Tarisi; Anayenera kupita ku Ofiri kukatenga golide, koma sanapite chifukwa zombozo zinasweka ku Ezioni Geberi. Pamenepo Ahaziya mwana wa Ahabu anauza Yehosafati kuti: “Atumiki anga apite limodzi ndi atumiki ako mzombo. Koma Yehosafati sanalole. Yehosafati anagona pamodzi ndi makolo ake, naikidwa pamodzi ndi makolo ake mu Mzinda wa Davide kholo lake; Yehoramu mwana wake anakhala mfumu mmalo mwake.
\v 48 Yehosafati anamanga zombo za ku Tarisi; Anayenera kupita ku Ofiri kukatenga golide, koma sanapite chifukwa zombozo zinasweka ku Ezioni Geberi. \v 49 Pamenepo Ahaziya mwana wa Ahabu anauza Yehosafati kuti: “Atumiki anga apite limodzi ndi atumiki ako mzombo. Koma Yehosafati sanalole. \v 50 Yehosafati anagona pamodzi ndi makolo ake, naikidwa pamodzi ndi makolo ake mu Mzinda wa Davide kholo lake; Yehoramu mwana wake anakhala mfumu mmalo mwake.

1
22/51.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 51 Ahaziya mwana wa Ahabu anakhala mfumu ya Isiraeli ku Samariya mchaka cha 17 cha Yehosafati mfumu ya Yuda, ndipo analamulira Isiraeli zaka ziwiri. \v 52 Iye anachita zoipa pamaso pa Yehova, ndipo anayenda mnjira ya bambo ake, mnjira ya mayi ake, ndi mnjira ya Yerobiamu mwana wa Nebati, imene anachimwitsa nayo Isiraeli. \v 53 Iye anatumikira Baala ndi kumlambira, moti anakwiyitsa Yehova Mulungu wa Isiraeli, monga mmene bambo ake anachitira.

View File

@ -418,6 +418,7 @@
"22-41",
"22-43",
"22-45",
"22-48",
"22-51"
]
}