1 line
463 B
Plaintext
1 line
463 B
Plaintext
\v 51 Ahaziya mwana wa Ahabu anakhala mfumu ya Isiraeli ku Samariya m’chaka cha 17 cha Yehosafati mfumu ya Yuda, ndipo analamulira Isiraeli zaka ziwiri. \v 52 Iye anachita zoipa pamaso pa Yehova, ndipo anayenda m’njira ya bambo ake, m’njira ya mayi ake, ndi m’njira ya Yerobiamu mwana wa Nebati, imene anachimwitsa nayo Isiraeli. \v 53 Iye anatumikira Baala ndi kum’lambira, moti anakwiyitsa Yehova Mulungu wa Isiraeli, monga mmene bambo ake anachitira. |