Sat Apr 20 2024 10:03:12 GMT+0200 (South Africa Standard Time)
This commit is contained in:
parent
c0f9861342
commit
bfe3ff5f4e
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 45 Nkhani zina zokhudza Yehosafati ndi mphamvu zimene anachita, ndi mmene anamenyera nkhondo, zinalembedwa m’buku la zochitika za mafumu a Yuda. \v 46 Anachotsa m’dziko mahule ena onse amene anatsala m’masiku a bambo ake Asa. \v 47 Munalibe mfumu ku Edomu koma wachiwiri wake ankalamulira kumeneko.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
Yehosafati anamanga zombo za ku Tarisi; Anayenera kupita ku Ofiri kukatenga golide, koma sanapite chifukwa zombozo zinasweka ku Ezioni Geberi. Pamenepo Ahaziya mwana wa Ahabu anauza Yehosafati kuti: “Atumiki anga apite limodzi ndi atumiki ako m’zombo. Koma Yehosafati sanalole. Yehosafati anagona pamodzi ndi makolo ake, naikidwa pamodzi ndi makolo ake mu Mzinda wa Davide kholo lake; Yehoramu mwana wake anakhala mfumu m’malo mwake.
|
|
@ -418,7 +418,6 @@
|
|||
"22-41",
|
||||
"22-43",
|
||||
"22-45",
|
||||
"22-48",
|
||||
"22-51"
|
||||
]
|
||||
}
|
Loading…
Reference in New Issue