Sat Apr 20 2024 10:01:10 GMT+0200 (South Africa Standard Time)
This commit is contained in:
parent
ad6b9fa6e3
commit
c0f9861342
|
@ -1 +1 @@
|
|||
\v 39 \v 40 Nkhani zina zokhudza Ahabu ndi zonse zimene anachita, nyumba ya minyanga ya njovu imene anamanga ndi mizinda yonse imene anamanga, zinalembedwa m’buku la zochitika za mafumu a Isiraeli kodi? Choncho Ahabu anagona pamodzi ndi makolo ake, ndipo Ahaziya mwana wake anayamba kulamulira m’malo mwake.
|
||||
\v 39 Nkhani zina zokhudza Ahabu ndi zonse zimene anachita, nyumba ya minyanga ya njovu imene anamanga ndi mizinda yonse imene anamanga, zinalembedwa m’buku la zochitika za mafumu a Isiraeli kodi? \v 40 Choncho Ahabu anagona pamodzi ndi makolo ake, ndipo Ahaziya mwana wake anayamba kulamulira m’malo mwake.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 41 Kenako Yehosafati mwana wa Asa anayamba kulamulira Yuda m’chaka chachinayi cha Ahabu mfumu ya Isiraeli. \v 42 Yehosafati anali wa zaka makumi atatu kudza zisanu polowa ufumu wace, nakhala mfumu m'Yerusalemu zaka makumi awiri mphambu zisanu. Dzina la amayi ake linali Azuba mwana wa Sili.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 43 Iye anayenda m’njira za atate wake Asa; sanapatuke kwa iwo; Iye anachita zoyenera pamaso pa Yehova. Koma misanje sinachotsedwe. Anthu anali kuperekabe nsembe ndi kufukiza pamisanje. \v 44 Yehosafati anachita mtendere ndi mfumu ya Isiraeli.
|
|
@ -414,6 +414,7 @@
|
|||
"22-34",
|
||||
"22-35",
|
||||
"22-37",
|
||||
"22-39",
|
||||
"22-41",
|
||||
"22-43",
|
||||
"22-45",
|
||||
|
|
Loading…
Reference in New Issue