Thu Apr 18 2024 11:40:18 GMT+0200 (South Africa Standard Time)
This commit is contained in:
parent
466f3a519e
commit
d16d328cec
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 16 Ana a Isiraeli anathawa pamaso pa Yuda, ndipo Yehova anawapereka m’manja mwa Yuda. \v 17 Abiya ndi ankhondo ake anawapha ndi kupha kwakukulu; Amuna osankhidwa a Isiraeli 500,000 anafa. \v 18 Momwemo anagonjetsedwa ana a Israyeli pa nthawiyo; Ana a Yuda anapambana chifukwa anadalira Yehova Mulungu wa makolo awo.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 19 Abiya anathamangitsa Yerobiamu; anamlanda midzi: Beteli ndi midzi yake, Yeshana ndi midzi yake, ndi Efroni ndi midzi yake. \v 20 Yerobiamu sanakhalenso ndi mphamvu masiku a Abiya; Yehova anamkantha, nafa. \v 21 Koma Abiya anakhala wamphamvu; anadzitengera akazi khumi ndi anayi, nabala ana amuna makumi awiri mphambu awiri, ndi ana akazi khumi ndi asanu ndi mmodzi. \v 22 Nkhani zina zokhudza Abiya, zochita zake ndi mawu ake, zinalembedwa m’buku la mbiri ya mneneri Ido.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
Mutu 14
|
|
@ -155,7 +155,6 @@
|
|||
"13-13",
|
||||
"13-16",
|
||||
"13-19",
|
||||
"14-title",
|
||||
"14-01",
|
||||
"14-05",
|
||||
"14-07",
|
||||
|
|
Loading…
Reference in New Issue