1 line
479 B
Plaintext
1 line
479 B
Plaintext
\v 19 Abiya anathamangitsa Yerobiamu; anamlanda midzi: Beteli ndi midzi yake, Yeshana ndi midzi yake, ndi Efroni ndi midzi yake. \v 20 Yerobiamu sanakhalenso ndi mphamvu masiku a Abiya; Yehova anamkantha, nafa. \v 21 Koma Abiya anakhala wamphamvu; anadzitengera akazi khumi ndi anayi, nabala ana amuna makumi awiri mphambu awiri, ndi ana akazi khumi ndi asanu ndi mmodzi. \v 22 Nkhani zina zokhudza Abiya, zochita zake ndi mawu ake, zinalembedwa m’buku la mbiri ya mneneri Ido. |