From d16d328cecf9e9beb8f53ec845781867e02f319c Mon Sep 17 00:00:00 2001 From: Muzgatama Date: Thu, 18 Apr 2024 11:40:19 +0200 Subject: [PATCH] Thu Apr 18 2024 11:40:18 GMT+0200 (South Africa Standard Time) --- 13/16.txt | 1 + 13/19.txt | 1 + 14/title.txt | 1 + manifest.json | 1 - 4 files changed, 3 insertions(+), 1 deletion(-) create mode 100644 13/16.txt create mode 100644 13/19.txt create mode 100644 14/title.txt diff --git a/13/16.txt b/13/16.txt new file mode 100644 index 0000000..2cb5075 --- /dev/null +++ b/13/16.txt @@ -0,0 +1 @@ +\v 16 Ana a Isiraeli anathawa pamaso pa Yuda, ndipo Yehova anawapereka m’manja mwa Yuda. \v 17 Abiya ndi ankhondo ake anawapha ndi kupha kwakukulu; Amuna osankhidwa a Isiraeli 500,000 anafa. \v 18 Momwemo anagonjetsedwa ana a Israyeli pa nthawiyo; Ana a Yuda anapambana chifukwa anadalira Yehova Mulungu wa makolo awo. \ No newline at end of file diff --git a/13/19.txt b/13/19.txt new file mode 100644 index 0000000..7a29055 --- /dev/null +++ b/13/19.txt @@ -0,0 +1 @@ +\v 19 Abiya anathamangitsa Yerobiamu; anamlanda midzi: Beteli ndi midzi yake, Yeshana ndi midzi yake, ndi Efroni ndi midzi yake. \v 20 Yerobiamu sanakhalenso ndi mphamvu masiku a Abiya; Yehova anamkantha, nafa. \v 21 Koma Abiya anakhala wamphamvu; anadzitengera akazi khumi ndi anayi, nabala ana amuna makumi awiri mphambu awiri, ndi ana akazi khumi ndi asanu ndi mmodzi. \v 22 Nkhani zina zokhudza Abiya, zochita zake ndi mawu ake, zinalembedwa m’buku la mbiri ya mneneri Ido. \ No newline at end of file diff --git a/14/title.txt b/14/title.txt new file mode 100644 index 0000000..e49eabc --- /dev/null +++ b/14/title.txt @@ -0,0 +1 @@ +Mutu 14 \ No newline at end of file diff --git a/manifest.json b/manifest.json index 1ba12b5..8e5a3f3 100644 --- a/manifest.json +++ b/manifest.json @@ -155,7 +155,6 @@ "13-13", "13-16", "13-19", - "14-title", "14-01", "14-05", "14-07",