Thu Jan 02 2020 18:53:53 GMT+0200 (South Africa Standard Time)

This commit is contained in:
Bshop2 2020-01-02 18:53:54 +02:00
parent 105a1219ee
commit aba1d290fa
8 changed files with 14 additions and 7 deletions

View File

@ -1 +1 @@
\v 13 \v 14 M'modzi wa akulu ananifunsa ine kuti, "ndani awa, omwe abvala mikanjo yoyera, ndipo achokera kuti?" Ninakamba nayeve kuti, "bwana, mudziwa" ndipo anati kwa ine, "Awa ndi anthu amene anachoka mu manzunzo yowawa. Awasha mikanjo yao na kuyayeretsa na magazi ya mwana wa nkhosa.
\v 13 M'modzi wa akulu ananifunsa ine kuti, "ndani awa, omwe abvala mikanjo yoyera, ndipo achokera kuti?" \v 14 Ninakamba nayeve kuti, "bwana, mudziwa" ndipo anati kwa ine, "Awa ndi anthu amene anachoka mu manzunzo yowawa. Awasha mikanjo yao na kuyayeretsa na magazi ya mwana wa nkhosa.

View File

@ -1 +1 @@
\v 15 \v 16 \v 17 Pa chifukwa ichi, ali pa maso pa mpando wa Mulungu, ndipo amiupembeza usana na usiku mu nyumba yake. Iye wamene ankhalaa pa mpando wa chimfumu azaika tenti yake pa iwo. Sazamveranso njala, kapena kumvera ludzu. Dzuwa sizawagwesa, kapena kutenthewa. Chifukwa mwana wa nkhosa pakati pa mpando azankhala mbusa wao, ndipo azawapereka ku malo a manzi ya moyo, ndipo Mulungu azapukuta misozi mu menso yao."
\v 15 Pa chifukwa ichi, ali pa maso pa mpando wa Mulungu, ndipo amiupembeza usana na usiku mu nyumba yake. Iye wamene ankhalaa pa mpando wa chimfumu azaika tenti yake pa iwo. \v 16 Sazamveranso njala, kapena kumvera ludzu. Dzuwa sizawagwesa, kapena kutenthewa. \v 17 Chifukwa mwana wa nkhosa pakati pa mpando azankhala mbusa wao, ndipo azawapereka ku malo a manzi ya moyo, ndipo Mulungu azapukuta misozi mu menso yao."

View File

@ -1 +1 @@
\c 8 \v 1 \v 2 Pamene mwana wa nkhosa anasegula chizindikiro cha namba 7, kunali chete ku mwamba kwa theka la ola limozi. Ndipo ninaona angelo 7 amene ankhala pa mpando wa chimfumu wa Mulungu, ndipo malipenga 7 yanapasidwa kwa iwo.
\c 8 \v 1 Pamene mwana wa nkhosa anasegula chizindikiro cha namba 7, kunali chete ku mwamba kwa theka la ola limozi. \v 2 Ndipo ninaona angelo 7 amene ankhala pa mpando wa chimfumu wa Mulungu, ndipo malipenga 7 yanapasidwa kwa iwo.

View File

@ -1 +1 @@
\v 3 \v 4 \v 5 Mngelo wina anabwera, ananyamula mbale ya golide ya zonunkhirisa, kuimilira pa guwa la zonunkhirisa. Zonunkhirisa zambiri zinapasidwa kwa iye kuti apereke pamozi na mapemphero ya okhulupilira pa guwa la zonunkhirisa pa mpando wa chimfumu. Utsi wa zonunkhirisa, na mapemphero ya okhulupirira, yanafikira ku mpando wa Mulungu kuchoka ku manja ya mngelo. Mngelo anatenga mbale ya zonunkhira na kuikamo moto wa pa guwa. Ndipo anaiponya pansi pa dziko la pansi, ndipo panali phokoso la kaleza, kugunda na kung'anipa kwa mphenzi, na chibvomezi.
\v 3 Mngelo wina anabwera, ananyamula mbale ya golide ya zonunkhirisa, kuimilira pa guwa la zonunkhirisa. Zonunkhirisa zambiri zinapasidwa kwa iye kuti apereke pamozi na mapemphero ya okhulupilira pa guwa la zonunkhirisa pa mpando wa chimfumu. \v 4 Utsi wa zonunkhirisa, na mapemphero ya okhulupirira, yanafikira ku mpando wa Mulungu kuchoka ku manja ya mngelo. \v 5 Mngelo anatenga mbale ya zonunkhira na kuikamo moto wa pa guwa. Ndipo anaiponya pansi pa dziko la pansi, ndipo panali phokoso la kaleza, kugunda na kung'anipa kwa mphenzi, na chibvomezi.

View File

@ -1 +1 @@
\v 6 \v 7 Angelo 7 omwe anali na malipenga anakonzeka kuti alize. Mngelo oyamba analiza lipenga lake, ndipo panali mvula ya mphepo, moto yosakaniza na magazi. Inaponyedwa pa dziko la pansi kwakuti gawo lina linatenthedwa, gawo la mitengo inapya, ndi udzu onse obiliwira unapya.
\v 6 Angelo 7 omwe anali na malipenga anakonzeka kuti alize. \v 7 Mngelo oyamba analiza lipenga lake, ndipo panali mvula ya mphepo, moto yosakaniza na magazi. Inaponyedwa pa dziko la pansi kwakuti gawo lina linatenthedwa, gawo la mitengo inapya, ndi udzu onse obiliwira unapya.

View File

@ -1 +1 @@
\v 8 \v 9 Mngelo wa chiwiri analiza lipenga lake, ndipo chinthu china chachikulu monga phiri chinaponyedwa mnyanja. Gawo lina la manzi inankhala magazi, zina mwa nyama za m'manzi zinafa, ndipo ma bwato ambiri anaonongeka.
\v 8 Mngelo wa chiwiri analiza lipenga lake, ndipo chinthu china chachikulu monga phiri chinaponyedwa mnyanja. Gawo lina la manzi inankhala magazi, \v 9 zina mwa nyama za m'manzi zinafa, ndipo ma bwato ambiri anaonongeka.

View File

@ -1 +1 @@
\v 10 \v 11 Mngelo wachitatu analiza lipenga lake, ndipo nyenyezi yaikulu inagwa kuchoka ku mwamba, yoyaka monga tochi, pa gawo lalikulu la misinje na nyenje za madzi. Dzina la nyenyezi ni chobaba. Ndipo madzi yanankhala yobaba, ndipo anthu ambiri anafa chifukwa cha manzi yobaba.
\v 10 Mngelo wachitatu analiza lipenga lake, ndipo nyenyezi yaikulu inagwa kuchoka ku mwamba, yoyaka monga tochi, pa gawo lalikulu la misinje na nyenje za madzi. \v 11 Dzina la nyenyezi ni chobaba. Ndipo madzi yanankhala yobaba, ndipo anthu ambiri anafa chifukwa cha manzi yobaba.

View File

@ -103,6 +103,13 @@
"07-07",
"07-09",
"07-11",
"07-13",
"07-15",
"08-title",
"08-01",
"08-03",
"08-06",
"08-08",
"10-01",
"10-03",
"10-05",