nya-x-nyanja_rev_text_reg/08/10.txt

1 line
280 B
Plaintext

\v 10 Mngelo wachitatu analiza lipenga lake, ndipo nyenyezi yaikulu inagwa kuchoka ku mwamba, yoyaka monga tochi, pa gawo lalikulu la misinje na nyenje za madzi. \v 11 Dzina la nyenyezi ni chobaba. Ndipo madzi yanankhala yobaba, ndipo anthu ambiri anafa chifukwa cha manzi yobaba.