nya-x-nyanja_rev_text_reg/08/08.txt

1 line
221 B
Plaintext

\v 8 Mngelo wa chiwiri analiza lipenga lake, ndipo chinthu china chachikulu monga phiri chinaponyedwa mnyanja. Gawo lina la manzi inankhala magazi, \v 9 zina mwa nyama za m'manzi zinafa, ndipo ma bwato ambiri anaonongeka.