Thu Apr 18 2024 15:27:04 GMT+0200 (South Africa Standard Time)
This commit is contained in:
parent
a7221d8822
commit
95565ff378
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 24 Mwana wamkazi wa Farao anachoka mumzinda wa Davide n’kupita ku nyumba imene Solomo anam’mangira. Pambuyo pake, Solomo anamanga Milo.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 25 Katatu caka ciliconse Solomo anali kupeleka nsembe zopsereza ndi zaciyanjano pa guwa lansembe limene anamangira Yehova, nafukiza nazo zofukiza pa guwa lansembe limene linali pamaso pa Yehova. Chotero anamaliza kachisi ndipo tsopano anali kuligwiritsa ntchito.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 26 Mfumu Solomo inamanga zombo zankhondo ku Ezioni Geberi, pafupi ndi Elati m’mphepete mwa Nyanja Yofiira m’dziko la Edomu. \v 27 Hiramu anatumiza atumiki ku zombo za Solomo, amalinyero odziwa bwino nyanja, pamodzi ndi antchito a Solomo. \v 28 Iwo anapita ku Ofiri pamodzi ndi atumiki a Solomo. Kumeneko anabweretsa matalente 420 agolide kwa Mfumu Solomo.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\c 10 \v 1 Mfumu yaikazi ya ku Sheba itamva za Solomo za dzina la Yehova, inadza kudzamuyesa ndi mafunso ovuta. \v 2 Iye anafika ku Yerusalemu ndi gulu lalitali kwambiri, ngamila zonyamula zonunkhira, golide wambiri, ndi miyala yamtengo wapatali. Atafika, anauza Solomo zonse zimene zinali mumtima mwake.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
Mutu 10
|
|
@ -206,11 +206,11 @@
|
|||
"09-17",
|
||||
"09-20",
|
||||
"09-22",
|
||||
"09-23",
|
||||
"09-24",
|
||||
"09-25",
|
||||
"09-26",
|
||||
"10-title",
|
||||
"10-01",
|
||||
"10-03",
|
||||
"10-06",
|
||||
"10-08",
|
||||
|
|
Loading…
Reference in New Issue