nya-x-nyanja_luk_text_reg/01/14.txt

1 line
241 B
Plaintext

\v 14 \v 15 Uzankhala na chimwemwe ndi chisangalalo, ndipo ambiri azamwetukila ku badwa kwake.Azankhala wamukulu pamanso ya Mulungu.Asakamwepo vinyu loko zozazamwa maningi, ndipo azazozedwa ndi muzimu oyela kuchokela mu mimba mwaba maibake.