\v 14 \v 15 Uzankhala na chimwemwe ndi chisangalalo, ndipo ambiri azamwetukila ku badwa kwake.Azankhala wamukulu pamanso ya Mulungu.Asakamwepo vinyu loko zozazamwa maningi, ndipo azazozedwa ndi muzimu oyela kuchokela mu mimba mwaba maibake.