nya-x-nyanja_rev_text_reg/20/11.txt

1 line
385 B
Plaintext

\v 11 ninaona mupando waukulu oyera na wamene anankhalapo. ziko lapansi na kumwamba kunathaba ulemelero wake, koma kunalibe malo yakuti zibisameko. \v 12 ninaona omwalira-ba mphamvu na opanda nchito-kuimilira pa mpando wa mfumu, mabuku yanaseguliwa. buku inangu inaseguliwa-buku la moyo. banthu bakufa banaweruziwa kulingana na zamene zinalembewa mu mabuku, kulingana na zinchito zawo.