nya-x-nyanja_sng_text_reg/07/07.txt

1 line
273 B
Plaintext

\v 7 Kutalimpa kwako kuli ngati mtengo wa kanjeza, ndipo mabele yako yali ngati gulu ya zipatso. \v 8 Ninakamba kuti, "Nifuna kukwela mutengo wa kanjeza; nizagwila misabo zake." Mabele yako yakhale ngati zipatso za mphesa, Ndipo fungoyla mphuno yako ikhale ngati apulikoti.