nya-x-nyanja_sng_text_reg/04/06.txt

1 line
173 B
Plaintext

\v 6 Mpaka mbandakucha ndi mithunzi ithawe, ndipita kuphiri la mure ndi kuphiri la lubani. \v 7 Ndiwe wokongola m'njira zonse, wokondedwa wanga ndipo palibe chilema mwa iwe.