nya-x-nyanja_sng_text_reg/03/08.txt

1 line
218 B
Plaintext

\v 8 Bonse ni bakaswili na lupanga ndipo nioziba nkhondo. Muntu aliyense ali na lupanga yake m'msana mwake, okonzekela ndi zoyofiya za usiku. \v 9 Mfumu Solomo anzipangira yekha mpando wamatabwa wochokera ku Lebanoni.