nya-x-nyanja_sng_text_reg/07/12.txt

1 line
185 B
Plaintext

\v 12 Tidzuke m'mawa kuti tipite kuminda yamphesa; tiwone ngati mipesa yaphuka, kaya maluwa ake atseguka; kapena ngati makangaza ali ndi maluŵa. Kumeneko ndidzakupatsa chikondi changa.