nya-x-nyanja_sng_text_reg/07/07.txt

1 line
275 B
Plaintext

\v 7 Kutalimpa kwako kuli kwati mutengo wa kanjeza, ndipo mabele yako yali kwati gulu ya ba paso. \v 8 Nina kamba kuti, "Nifuna kukwela mutengo wa kanjeza; nizagwila misabo zake." Mabele yako ya nkale kwati zipatso za mphesa, Ndipo fungoyla mpuno yako inkale kwati apulikoti.