nya-x-nyanja_sng_text_reg/02/12.txt

1 line
288 B
Plaintext

\v 12 Maluwa yaonekela paziko ya pansi; ntawi yodulia na kuimba kwa nyoni yafika, ndipo phokoso ya nkunda ya mveka mu ziko yatu. \v 13 Mutengo wa mukuyu yapya nkuyu wake yobiliwila, ndipo mipesa yachita maluba; zipeleka fungo yake. Nyamuka, okodewa wanga, okongola wanga, tiye tiziyenda.