Thu Jan 02 2020 19:07:53 GMT+0200 (South Africa Standard Time)

This commit is contained in:
Bshop2 2020-01-02 19:07:54 +02:00
parent 6a37c2e144
commit 8f552b2a4a
13 changed files with 32 additions and 13 deletions

View File

@ -1 +1 @@
\v 17 \v 18 ninaona mungelo oimilira pa zuba. anaitana na mau yamphamvu ku nyoni zonse zouluka mumwamba, "bwerani, munkhale pamozi ku pwando la mulungu. bwerani mudye matupi ya mamfumu, matupi ya akulu a nkhondo, matupi ya banthu ba mphamvu, matupi ya mahosi na bamene bakwerapo, na matupi ya banthu bonse, akapolo na omasuka, banthu bopanda nchito na ba mphamvu."
\v 17 ninaona mungelo oimilira pa zuba. anaitana na mau yamphamvu ku nyoni zonse zouluka mumwamba, "bwerani, munkhale pamozi ku pwando la mulungu. \v 18 bwerani mudye matupi ya mamfumu, matupi ya akulu a nkhondo, matupi ya banthu ba mphamvu, matupi ya mahosi na bamene bakwerapo, na matupi ya banthu bonse, akapolo na omasuka, banthu bopanda nchito na ba mphamvu."

View File

@ -1 +1 @@
\v 19 \v 20 ninaona chilombo na mamfumu ba pa ziko lapansi na banthu babo ba nkhondo. banakumana kuti bamenye nkhondo na baja bali pa mahosi na bankhondo bake. chilombo chinagwiliwa pamozi na mneneri waboza wamene anachita zodabwisa pamenso pake. na zizindikiro zamene izi ananamiza bonse bamene banalandira cizindikiro cha chilombo na bamene banapembeza chifano chake. bonse babili banaponyedwa mu nyanja ya muliro wa sufule.
\v 19 ninaona chilombo na mamfumu ba pa ziko lapansi na banthu babo ba nkhondo. banakumana kuti bamenye nkhondo na baja bali pa mahosi na bankhondo bake. \v 20 chilombo chinagwiliwa pamozi na mneneri waboza wamene anachita zodabwisa pamenso pake. na zizindikiro zamene izi ananamiza bonse bamene banalandira cizindikiro cha chilombo na bamene banapembeza chifano chake. bonse babili banaponyedwa mu nyanja ya muliro wa sufule.

View File

@ -1 +1 @@
\v 7 \v 8 pamene zaka 1000 zisila, satana azamumasula ku ndende yake. azayenda kunamiza maiko mbali zonse za ziko lapansi-gog na magog kubaleta pamozi kuti bamenye nkhondo. bazankhala bambiri kwati ni dothi la mu manzi.
\v 7 pamene zaka 1000 zisila, satana azamumasula ku ndende yake. \v 8 azayenda kunamiza maiko mbali zonse za ziko lapansi-gog na magog kubaleta pamozi kuti bamenye nkhondo. bazankhala bambiri kwati ni dothi la mu manzi.

View File

@ -1 +1 @@
\v 11 \v 12 ninaona mupando waukulu oyera na wamene anankhalapo. ziko lapansi na kumwamba kunathaba ulemelero wake, koma kunalibe malo yakuti zibisameko. ninaona omwalira-ba mphamvu na opanda nchito-kuimilira pa mpando wa mfumu, mabuku yanaseguliwa. buku inangu inaseguliwa-buku la moyo. banthu bakufa banaweruziwa kulingana na zamene zinalembewa mu mabuku, kulingana na zinchito zawo.
\v 11 ninaona mupando waukulu oyera na wamene anankhalapo. ziko lapansi na kumwamba kunathaba ulemelero wake, koma kunalibe malo yakuti zibisameko. \v 12 ninaona omwalira-ba mphamvu na opanda nchito-kuimilira pa mpando wa mfumu, mabuku yanaseguliwa. buku inangu inaseguliwa-buku la moyo. banthu bakufa banaweruziwa kulingana na zamene zinalembewa mu mabuku, kulingana na zinchito zawo.

View File

@ -1 +1 @@
\v 13 \v 14 \v 15 nyanja zinachosa bamene banaferamo. imfa na hadesi zinachosa bakufa bamene banalimo, elo bakufa banaweruziwa kulingana na zamene banachita. imfa na hadesi zinaponyewa mu nyanja ya muliro. uku nikufa kwa chiwiri- nyanja ya muliro. ngati zina ya wina aliyense sinalembewe mu buku la moyo, anaponyewa mu nyanja ya muliro.
\v 13 nyanja zinachosa bamene banaferamo. imfa na hadesi zinachosa bakufa bamene banalimo, elo bakufa banaweruziwa kulingana na zamene banachita. \v 14 imfa na hadesi zinaponyewa mu nyanja ya muliro. uku nikufa kwa chiwiri- nyanja ya muliro. \v 15 ngati zina ya wina aliyense sinalembewe mu buku la moyo, anaponyewa mu nyanja ya muliro.

View File

@ -1 +1 @@
\c 21 \v 1 \v 2 elo ninaona kumwamba kwasopano na ziko lapansi lasopano, cifukwa kumwamba na ziko ya kudala vinapita, na nyanja sizinaliko. ninaona muzinda oyera, yerusalemu wa sopano, zamene zinachoka kumwamba kwa mulungu, kukonzewa monga mkazi wamene akumana na mwamuna wake.
\c 21 \v 1 elo ninaona kumwamba kwasopano na ziko lapansi lasopano, cifukwa kumwamba na ziko ya kudala vinapita, na nyanja sizinaliko. \v 2 ninaona muzinda oyera, yerusalemu wa sopano, zamene zinachoka kumwamba kwa mulungu, kukonzewa monga mkazi wamene akumana na mwamuna wake.

View File

@ -1 +1 @@
\v 3 \v 4 ninamvera mau yochokera ku mpando kukamba kuti, "onani! malo yamene mulungu ankhalako yali na banthu, elo azankhala nabeve. bazankhala banthu bake, elo mulungu mwini wake azankhala nabeve elo azankhala mulungu wao. azapukuta misozi yawo yonse mumenso mwawo, elo sikuzankhala kufa, kulira, kapena kudandaula, kapena kuwawa. zinthu zakudala zapita.
\v 3 ninamvera mau yochokera ku mpando kukamba kuti, "onani! malo yamene mulungu ankhalako yali na banthu, elo azankhala nabeve. bazankhala banthu bake, elo mulungu mwini wake azankhala nabeve elo azankhala mulungu wao. \v 4 azapukuta misozi yawo yonse mumenso mwawo, elo sikuzankhala kufa, kulira, kapena kudandaula, kapena kuwawa. zinthu zakudala zapita.

View File

@ -1 +1 @@
\v 5 \v 6 wamene anankhala pa mpando anakamba ati, "ona! nipanga zinthu zonse zasopano." anati, "lemba izi pansi chifukwa mau aya ni ya zoona." anakamba naine ati, "izi zinthu zasila! ndine alefa na omega, oyamba na osiliza. kwa wamene amvera njota nizamupasa manzi yosagula kuchoka ku musinje wa manzi ya moyo.
\v 5 wamene anankhala pa mpando anakamba ati, "ona! nipanga zinthu zonse zasopano." anati, "lemba izi pansi chifukwa mau aya ni ya zoona." \v 6 anakamba naine ati, "izi zinthu zasila! ndine alefa na omega, oyamba na osiliza. kwa wamene amvera njota nizamupasa manzi yosagula kuchoka ku musinje wa manzi ya moyo.

View File

@ -1 +1 @@
\v 7 \v 8 wamene apambana azatenga zinthu zimenezi, elo ine nizankhala mulungu wake, yeve azankhala mwana wanga. koma bamene bachita mantha, opanda chikulupiliro, na okanika, wopaya anzao, bachigololo, ba boza, opembeza mafano malo yawo ni ku nyanja ya muliro wa sufule. iyi ni imfa ya chiwiri."
\v 7 wamene apambana azatenga zinthu zimenezi, elo ine nizankhala mulungu wake, yeve azankhala mwana wanga. \v 8 koma bamene bachita mantha, opanda chikulupiliro, na okanika, wopaya anzao, bachigololo, ba boza, opembeza mafano malo yawo ni ku nyanja ya muliro wa sufule. iyi ni imfa ya chiwiri."

View File

@ -1 +1 @@
\v 9 \v 10 m'mozi wa angelo bali 7 anabwera kwa ine, wamene anali na mbale 7 zozula na zilango zosiliza, anakamba kwa ine, "bwera kuno. nizakulangiza mkazi, mkazi wa mwana wa nkhosa." ananitenga mu mzimu kuyenda ku lupili itali nakunilangiza muzinda oyera yerusalemu kuseluka kuchoka ku mwamba kwa mulungu.
\v 9 m'mozi wa angelo bali 7 anabwera kwa ine, wamene anali na mbale 7 zozula na zilango zosiliza, anakamba kwa ine, "bwera kuno. nizakulangiza mkazi, mkazi wa mwana wa nkhosa." \v 10 ananitenga mu mzimu kuyenda ku lupili itali nakunilangiza muzinda oyera yerusalemu kuseluka kuchoka ku mwamba kwa mulungu.

View File

@ -1 +1 @@
\v 11 \v 12 \v 13 yerusalemu anali na ulemelero wa mulungu, na kuwala kwake kunali monga mphete, monga mwala wa bafuta wa jesipa. unali na mpanda waukulu, na polowera 12, na angelo pa khomo. pa makomo onse panalembewa maina ya mitundu 12 ya ana a israele. ku m'mawa kunali makomo atatu, kumpoto kunali makomo atatu, ku m'mwera kunali makomo atatu komanspo kumazulo kunali makomo atatu.
\v 11 yerusalemu anali na ulemelero wa mulungu, na kuwala kwake kunali monga mphete, monga mwala wa bafuta wa jesipa. \v 12 unali na mpanda waukulu, na polowera 12, na angelo pa khomo. pa makomo onse panalembewa maina ya mitundu 12 ya ana a israele. \v 13 ku m'mawa kunali makomo atatu, kumpoto kunali makomo atatu, ku m'mwera kunali makomo atatu komanspo kumazulo kunali makomo atatu.

View File

@ -1 +1 @@
\v 14 \v 15 mpanda wa mzinda unali ni maziko 12, pa izo panali maina 12 ya apositoli a mwana wa nkhosa. wamene anakamba na ine anali na kopimila kopangiwa na golide kamene anapimila mzinda, makomo na mpanda wake.
\v 14 mpanda wa mzinda unali ni maziko 12, pa izo panali maina 12 ya apositoli a mwana wa nkhosa. \v 15 wamene anakamba na ine anali na kopimila kopangiwa na golide kamene anapimila mzinda, makomo na mpanda wake.

View File

@ -195,6 +195,25 @@
"19-07",
"19-09",
"19-11",
"19-14"
"19-14",
"19-17",
"19-19",
"19-21",
"20-title",
"20-01",
"20-04",
"20-05",
"20-07",
"20-09",
"20-11",
"20-13",
"21-title",
"21-01",
"21-03",
"21-05",
"21-07",
"21-09",
"21-11",
"21-14"
]
}