Thu Jan 02 2020 19:05:53 GMT+0200 (South Africa Standard Time)

This commit is contained in:
Bshop2 2020-01-02 19:05:54 +02:00
parent 1e484db11d
commit 6a37c2e144
11 changed files with 24 additions and 11 deletions

View File

@ -1 +1 @@
\v 15 \v 17 katundu wa aba bamene banalemela kamba ka uyu uzaimilira kutali kamba ka mantha ya kuvutisiwa, kulira mokuwa. \v 16 bazakamba, ̈ tsoka, tsoka ku mzinda wampamvu wamene wenze unavalikiwa zovala zabwino, zabafuta komanso za golide, mphete zabwino! pa ola imozi chabe katundu onse waonongeka.̈ osogolera aliyense wa bwato, aliyense oyendesa bwato na aliyense amene ankhalira zinthu zamene zinkhala pa manzi, zinaimilira patali.
\v 15 katundu wa aba bamene banalemela kamba ka uyu uzaimilira kutali kamba ka mantha ya kuvutisiwa, kulira mokuwa. \v 16 bazakamba, ̈ tsoka, tsoka ku mzinda wampamvu wamene wenze unavalikiwa zovala zabwino, zabafuta komanso za golide, mphete zabwino! \v 17 pa ola imozi chabe katundu onse waonongeka.̈ osogolera aliyense wa bwato, aliyense oyendesa bwato na aliyense amene ankhalira zinthu zamene zinkhala pa manzi, zinaimilira patali.

View File

@ -1 +1 @@
\v 18 \v 19 \v 20 banalira pamene banaona chusi cha kupya kwake. banakamba ati, ̈ ni muzinda wabwanji wamene uli ngati muzinda wampamvu?̈ bataya dothi pa mitu zao, na kulira mwampamvu, ̈ tsoka, tsoka ku muzinda wa mphamvu wamene bonse benzeli na bwato banalemela na chuma chake. pakuti pa ola imozi chabe aonongeka.̈ kondwerani na yeve, kumwamba, inu okulupilira, atumwi na apolofeti, pakuti mulungu abweresa chiweruzo pa yeve!̈
\v 18 banalira pamene banaona chusi cha kupya kwake. banakamba ati, ̈ ni muzinda wabwanji wamene uli ngati muzinda wampamvu?̈ \v 19 bataya dothi pa mitu zao, na kulira mwampamvu, ̈ tsoka, tsoka ku muzinda wa mphamvu wamene bonse benzeli na bwato banalemela na chuma chake. pakuti pa ola imozi chabe aonongeka.̈ \v 20 kondwerani na yeve, kumwamba, inu okulupilira, atumwi na apolofeti, pakuti mulungu abweresa chiweruzo pa yeve!̈

View File

@ -1 +1 @@
\v 21 \v 22 mungelo wamphamvu anatenga mwala owoneka kwati ni chogailapo na kuuponya mu manzi, kukamba ati, ̈ pa sochabe, babylon, muzinda wa mpamvu uzaponyedwa na ndewo zake ndipo suzaonekanso.zoimba zopangidwa ndi oliza mitolilo, oimba nyimbo ndi malipenga sazamvekaso pa inu. palibe munthu aliyense wa maluso sazapezeka pakati panu. palibe chigayo chamene chizamveka pakati panu.
\v 21 mungelo wamphamvu anatenga mwala owoneka kwati ni chogailapo na kuuponya mu manzi, kukamba ati, ̈ pa sochabe, babylon, muzinda wa mpamvu uzaponyedwa na ndewo zake ndipo suzaonekanso. \v 22 Zoimba zopangidwa ndi oliza mitolilo, oimba nyimbo ndi malipenga sazamvekaso pa inu. palibe munthu aliyense wa maluso sazapezeka pakati panu. palibe chigayo chamene chizamveka pakati panu.

View File

@ -1 +1 @@
\v 23 \v 24 nyale sizawalanso pakati panu. mau ya mkwati ndi mkwatibwi siyazamvekanso pa inu, pakuti banthu banu banali mamfumu pa ziko lapansi, elo maiko yananamiziwa na ung'anga wanu. muli yeve magazi ya aneneri na okulupilira yanapezeka, na magazi ya onse bamene banapaiwa pa ziko.̈
\v 23 nyale sizawalanso pakati panu. mau ya mkwati ndi mkwatibwi siyazamvekanso pa inu, pakuti banthu banu banali mamfumu pa ziko lapansi, elo maiko yananamiziwa na ung'anga wanu. \v 24 muli yeve magazi ya aneneri na okulupilira yanapezeka, na magazi ya onse bamene banapaiwa pa ziko.̈

View File

@ -1 +1 @@
\c 19 \v 1 \v 2 zitapita izi zinthu ninamvera chamene chinamveka kwati ni mau yampamvu ya banthu bambiri kumwamba kukamba ati, "hallelujah. chipulumuso, ulemelero na mpamvu zikhale kwa mulungu wathu. chiweluzo chake ni chachilungamo na choona, cifukwa aweluza hule ya mpamvu yamene inasokoneza ziko la pansi na nkhalidwe yake ya uhule. wabwezera magazi ya akapolo ake, yamene iye anakhesa."
\c 19 \v 1 zitapita izi zinthu ninamvera chamene chinamveka kwati ni mau yampamvu ya banthu bambiri kumwamba kukamba ati, "hallelujah. chipulumuso, ulemelero na mpamvu zikhale kwa mulungu wathu. \v 2 chiweluzo chake ni chachilungamo na choona, cifukwa aweluza hule ya mpamvu yamene inasokoneza ziko la pansi na nkhalidwe yake ya uhule. wabwezera magazi ya akapolo ake, yamene iye anakhesa."

View File

@ -1 +1 @@
\v 3 \v 4 banakamba kaciwiri: "hallelujah! chusi chamene chichoka kwa yeve muyayaya." akulu 24 na zamoyo 4 zinagwa pansi na kupembeza mulungu amene anali nkhale pa mpando wa chimfumu. banali kukamba ati, "zinkhale tero. hallelujah!"
\v 3 banakamba kaciwiri: "hallelujah! chusi chamene chichoka kwa yeve muyayaya." \v 4 akulu 24 na zamoyo 4 zinagwa pansi na kupembeza mulungu amene anali nkhale pa mpando wa chimfumu. banali kukamba ati, "zinkhale tero. hallelujah!"

View File

@ -1 +1 @@
\v 7 \v 8 tiyeni tikondwere na kunkhala okondwa na kumupasa ulemu chifukwa chisangalalo cha ukwati wa mwana wa nkhosa chafika, elo mkazi wa chikwati wakonzeka. analoledwa kuti abvale zovala zowala na zopanda dothi" (chifukwa zovala zopanda dothi ni zincito za anthu oyera).
\v 7 tiyeni tikondwere na kunkhala okondwa na kumupasa ulemu chifukwa chisangalalo cha ukwati wa mwana wa nkhosa chafika, elo mkazi wa chikwati wakonzeka. \v 8 Analoledwa kuti abvale zovala zowala na zopanda dothi" (chifukwa zovala zopanda dothi ni zincito za anthu oyera).

View File

@ -1 +1 @@
\v 9 \v 10 mungelo anakamba kwa ine, "lemba izi: ni odala amene aitaniwa ku pwando la ukwati wa mwana wa nkhosa." anakamba futi kwa ine ati, "aya ni mau ya zoona ya mulungu." ninagwa pansi pa mapazi ake kuti nimupembeze, koma anakamba kwa ine ati, "osachita tero! naine ndine kapolo kwati iwe na abale ako amene ali na umboni wa yesu. pembeza mulungu, pakuti umboni wa yesu ni muzimu wa uneneri."
\v 9 mungelo anakamba kwa ine, "lemba izi: ni odala amene aitaniwa ku pwando la ukwati wa mwana wa nkhosa." anakamba futi kwa ine ati, "aya ni mau ya zoona ya mulungu." \v 10 ninagwa pansi pa mapazi ake kuti nimupembeze, koma anakamba kwa ine ati, "osachita tero! naine ndine kapolo kwati iwe na abale ako amene ali na umboni wa yesu. pembeza mulungu, pakuti umboni wa yesu ni muzimu wa uneneri."

View File

@ -1 +1 @@
\v 11 \v 12 \v 13 elo ninaona kumwamba kuseguka, ninayangana kunali hosi yoyera. wamene analipo ni ozibika na zina yakuti okulupilika na wazoona. ni pa chilungamo kuti aweruza na kumenya nkhondo. menso yake yali ngati muliro, elo pa mpumi pake pali makolona yambiri. ali na zina yolembewa pa yeve yamene kulibe amene aziba koma yeve yeka. avala mukanjo wamene unafakiwa mu magazi, na zina lake ni mau ya mulungu.
\v 11 elo ninaona kumwamba kuseguka, ninayangana kunali hosi yoyera. wamene analipo ni ozibika na zina yakuti okulupilika na wazoona. ni pa chilungamo kuti aweruza na kumenya nkhondo. \v 12 menso yake yali ngati muliro, elo pa mpumi pake pali makolona yambiri. ali na zina yolembewa pa yeve yamene kulibe amene aziba koma yeve yeka. \v 13 avala mukanjo wamene unafakiwa mu magazi, na zina lake ni mau ya mulungu.

View File

@ -1 +1 @@
\v 14 \v 15 \v 16 basilikali ba kumwamba banali kumulondola pa mahosi yoyera, ovala zovala zabwino, zoyera elo zopanda dothi. mukamwa mwake muchoka mupeni wakutwa wamene amenyera maiko, azalamulira maiko na mphamvu. anaponda mothwela mpesa mu kukalipa kwa mulungu wa mphamvu. ali na zina yolembewa pa chovala chake na pa chibelo chake: "mfumu ya mamfumu na mbuye wa ambuye."
\v 14 basilikali ba kumwamba banali kumulondola pa mahosi yoyera, ovala zovala zabwino, zoyera elo zopanda dothi. \v 15 mukamwa mwake muchoka mupeni wakutwa wamene amenyera maiko, azalamulira maiko na mphamvu. anaponda mothwela mpesa mu kukalipa kwa mulungu wa mphamvu. \v 16 ali na zina yolembewa pa chovala chake na pa chibelo chake: "mfumu ya mamfumu na mbuye wa ambuye."

View File

@ -182,6 +182,19 @@
"18-07",
"18-09",
"18-11",
"18-14"
"18-14",
"18-15",
"18-18",
"18-21",
"18-23",
"19-title",
"19-01",
"19-03",
"19-05",
"19-06",
"19-07",
"19-09",
"19-11",
"19-14"
]
}