nya-x-nyanja_rev_text_reg/18/21.txt

1 line
384 B
Plaintext

\v 21 mungelo wamphamvu anatenga mwala owoneka kwati ni chogailapo na kuuponya mu manzi, kukamba ati, ̈ pa sochabe, babylon, muzinda wa mpamvu uzaponyedwa na ndewo zake ndipo suzaonekanso. \v 22 Zoimba zopangidwa ndi oliza mitolilo, oimba nyimbo ndi malipenga sazamvekaso pa inu. palibe munthu aliyense wa maluso sazapezeka pakati panu. palibe chigayo chamene chizamveka pakati panu.