Thu Jan 02 2020 18:46:41 GMT+0200 (South Africa Standard Time)

This commit is contained in:
Bshop2 2020-01-02 18:46:42 +02:00
parent a346b7e9da
commit 3b24623e76
9 changed files with 18 additions and 8 deletions

View File

@ -1 +1 @@
\v 26 \v 27 \v 28 \v 29 Wamene apambana nakuchita zamene nachita mpaka pothera, kwa yeve nizapasa ulamuliro pa maiko onse. Azalamulira maiko na mphamvu, azabapwanya monga mbiya ya dothi. Monga mwamene nalandilira kuli atate, nizamupasaso naine nyenyezi ya m'mawa. Lekani wamene ali na matu amvere zamene mzimu ukamba kwa mipingo.
\v 26 Wamene apambana nakuchita zamene nachita mpaka pothera, kwa yeve nizapasa ulamuliro pa maiko onse. \v 27 Azalamulira maiko na mphamvu, azabapwanya monga mbiya ya dothi. \v 28 Monga mwamene nalandilira kuli atate, nizamupasaso naine nyenyezi ya m'mawa. \v 29 Lekani wamene ali na matu amvere zamene mzimu ukamba kwa mipingo.

View File

@ -1 +1 @@
\c 3 \v 1 \v 2 "Kwa mngelo wa ku Sardis lemba: Aya ni mau ya wamene asunga mizimu 7 ya Mulungu na nyenyezi 7." Niziba zamene mwachita. Muli na mbiri yakuti muli na moyo, koma ndinu bakufa. Ukani na kulimbisa zamene zankhalako, koma zifuna kufa, chifukwa sininapezeko nchito iliyonse yabwino pamaso pa Mulungu wanga.
\c 3 \v 1 "Kwa mngelo wa ku Sardis lemba: Aya ni mau ya wamene asunga mizimu 7 ya Mulungu na nyenyezi 7." Niziba zamene mwachita. Muli na mbiri yakuti muli na moyo, koma ndinu bakufa. \v 2 Ukani na kulimbisa zamene zankhalako, koma zifuna kufa, chifukwa sininapezeko nchito iliyonse yabwino pamaso pa Mulungu wanga.

View File

@ -1 +1 @@
\v 3 \v 4 Kumbukirani, sopano, zamene munalandira na kumvera. Gonjerani, na kulapa. Koma ngati simuzauka, nizabwera monga kawalala, elo simuzaziba nthawi yamene nizabwelera kwa inu. Koma pali maina yang'ono chabe ya banthu mu Sardis bamene sibanafipise vovala vao. Bazayenda naine, mu zobvala zoyera, chifukwa nioyenera.
\v 3 Kumbukirani, sopano, zamene munalandira na kumvera. Gonjerani, na kulapa. Koma ngati simuzauka, nizabwera monga kawalala, elo simuzaziba nthawi yamene nizabwelera kwa inu. \v 4 Koma pali maina yang'ono chabe ya banthu mu Sardis bamene sibanafipise vovala vao. Bazayenda naine, mu zobvala zoyera, chifukwa nioyenera.

View File

@ -1 +1 @@
\v 5 \v 6 Wamene apambana azapasiwa zobvala zoyera, elo sinizachosa dzina lake mu buku la moyo, ndipo nizakamba za dzina lake kwa atate, na angelo ao. Lekani amene ali na matu amvere zamene mzimu akamba ku mipingo.
\v 5 Wamene apambana azapasiwa zobvala zoyera, elo sinizachosa dzina lake mu buku la moyo, ndipo nizakamba za dzina lake kwa atate, na angelo ao. \v 6 Lekani amene ali na matu amvere zamene mzimu akamba ku mipingo.

View File

@ -1 +1 @@
\v 9 \v 10 \v 11 Onani! onse amene achokera ku mpingo wa satana, iwo amene akamba ati ni bayuda koma sibayuda; anama chabe boza. Nizabapanga kuti babwere bagwade pa mapazi yanu, ndipo bazaziba kuti nikukondani. Chifukwa mwasunga malamulo anga mopilira, naine nizakusungani pa nthawi ya mayeso yamene ibwera padziko lapansi, kuyesa onse amene ankhala pa dziko. Nibwera manje-manje. Sungani bwino zamene muli nazo kuti anthu asalande kolona yanu.
\v 9 Onani! onse amene achokera ku mpingo wa satana, iwo amene akamba ati ni bayuda koma sibayuda; anama chabe boza. Nizabapanga kuti babwere bagwade pa mapazi yanu, ndipo bazaziba kuti nikukondani. \v 10 Chifukwa mwasunga malamulo anga mopilira, naine nizakusungani pa nthawi ya mayeso yamene ibwera padziko lapansi, kuyesa onse amene ankhala pa dziko. \v 11 Nibwera manje-manje. Sungani bwino zamene muli nazo kuti anthu asalande kolona yanu.

View File

@ -1 +1 @@
\v 12 \v 13 Nizapanga amene alimbikira kunkhala nsandamila ya mnyumba ya Mulungu, ndipo sazatulukamo. Nizalemba dzina la Mulungu pa iye, dzina la mzinda wa Mulungu wanga (Yerusalemu wasopano, wamene uchoka kumwamba kwa Mulungu wanga), na dzina langa lasopano. Lekani wamene ali na matu amvere zamene mzimu ukamba ku mipingo.
\v 12 Nizapanga amene alimbikira kunkhala nsandamila ya mnyumba ya Mulungu, ndipo sazatulukamo. Nizalemba dzina la Mulungu pa iye, dzina la mzinda wa Mulungu wanga (Yerusalemu wasopano, wamene uchoka kumwamba kwa Mulungu wanga), na dzina langa lasopano. \v 13 Lekani wamene ali na matu amvere zamene mzimu ukamba ku mipingo.

View File

@ -1 +1 @@
\v 14 \v 15 \v 16 Kwa mngelo wa mpingo wa ku Laodicea lemba: Aya ni mau ya ma Amen, mboni ya zoona na yodalilika, olamulira chilengedwe cha Mulung u. Niziba zamene mwachita, kuti sindinu otentha kapena ozizira. Chinakankhala bwino kuti munali otentha kapena ozizira! Tsono, chifukwa muli pakati-kati- simuli otentha kapena ozizira- nizakulabvulani mkamwa mwanga.
\v 14 Kwa mngelo wa mpingo wa ku Laodicea lemba: Aya ni mau ya ma Amen, mboni ya zoona na yodalilika, olamulira chilengedwe cha Mulung u. \v 15 Niziba zamene mwachita, kuti sindinu otentha kapena ozizira. Chinakankhala bwino kuti munali otentha kapena ozizira! Tsono, \v 16 chifukwa muli pakati-kati- simuli otentha kapena ozizira- nizakulabvulani mkamwa mwanga.

View File

@ -1 +1 @@
\v 17 \v 18 Mukamba kuti, ndinu olemera, nili na zinthu zambiri, ndipo sinifuna kalikonse. Koma simuziba kuti ndinu ochitisa chifundo maningi, osauka, osapenya ni osabvala. Mvelani zamene nikamba: Gulani kwa ine golide oikidwa mu moto kuti munkhale olemera na zobvala zoyera zowala kuti mubvale musaonese manyazi ya umaliseche wanu, na mankhwala ya m'maso kuti uone bwino.
\v 17 Mukamba kuti, ndinu olemera, nili na zinthu zambiri, ndipo sinifuna kalikonse. Koma simuziba kuti ndinu ochitisa chifundo maningi, osauka, osapenya ni osabvala. \v 18 Mvelani zamene nikamba: Gulani kwa ine golide oikidwa mu moto kuti munkhale olemera na zobvala zoyera zowala kuti mubvale musaonese manyazi ya umaliseche wanu, na mankhwala ya m'maso kuti uone bwino.

View File

@ -63,6 +63,16 @@
"02-18",
"02-20",
"02-22",
"02-24",
"02-26",
"03-title",
"03-01",
"03-03",
"03-05",
"03-09",
"03-12",
"03-14",
"03-17",
"10-01",
"10-03",
"10-05",