nya-x-nyanja_rev_text_reg/03/12.txt

1 line
324 B
Plaintext

\v 12 Nizapanga amene alimbikira kunkhala nsandamila ya mnyumba ya Mulungu, ndipo sazatulukamo. Nizalemba dzina la Mulungu pa iye, dzina la mzinda wa Mulungu wanga (Yerusalemu wasopano, wamene uchoka kumwamba kwa Mulungu wanga), na dzina langa lasopano. \v 13 Lekani wamene ali na matu amvere zamene mzimu ukamba ku mipingo.