nya-x-nyanja_mrk_text_reg/05/35.txt

1 line
188 B
Plaintext

\v 35 Pamene anali kulankhula naye, anthu ena anabwela kucokela kunyumba ya uja mtsogoleli wa sunagogi, nati, "mwana wanu mkazi wamwalila. Cifukwa ncani mupitiliza kumuvutisha mphunzitsi?"