Sat Oct 02 2021 08:23:12 GMT+0200 (Central Africa Time)
This commit is contained in:
parent
30fbd012dc
commit
eae178725b
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\c 45 \v 1 Atero Yehova kwa wodzozedwa wake, kwa Koresi, amene ndagwira dzanja lake lamanja, kuti ndigonjetse mitundu pamaso pake, kulanda mafumu zida, ndi kutsegula zitseko pamaso pake, kuti zipata zikhale zotseguka:
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 2 "Ndidzakutsogolera ndi kuyeza mapiri; ndidzathyola zitseko zamkuwa ndikuduladula mipiringidzo yawo yachitsulo, \v 3 ndipo ndidzakupatsa chuma cha mdima ndi chuma chobisika, kuti udziwe kuti ine ndine Inu Yehova, amene mumatchula dzina lanu, Ine ndine Mulungu wa Israyeli.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 4 Chifukwa cha Yakobo mtumiki wanga, ndi Israyeli wosankhidwa wanga, ndakutchula dzina lako, ndakupatsa ulemu, ngakhale sunandidziwa. \v 5 Ine ndine Yehova, palibenso wina; palibenso Mulungu wina koma Ine ndekha. Ndikumangira nkhondo, ngakhale sunandidziwe; \v 6 kuti anthu adziwe kuturukira dzuwa ndi kumadzulo, kuti palibe mulungu wina koma Ine; Ine ndine Yehova, ndipo palibenso wina.
|
|
@ -539,6 +539,8 @@
|
|||
"44-26",
|
||||
"44-28",
|
||||
"45-title",
|
||||
"45-01",
|
||||
"45-02",
|
||||
"49-title",
|
||||
"49-01",
|
||||
"49-03",
|
||||
|
|
Loading…
Reference in New Issue