Fri Oct 01 2021 22:14:41 GMT+0200 (Central Africa Time)
This commit is contained in:
parent
0a4a37ee78
commit
30fbd012dc
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 20 Uwona zinthu zambiri, koma osazindikira; makutu ali otseguka, koma palibe amene akumva. \v 21 Zinakondweretsa Yehova kutamanda chilungamo chake ndi kupangitsa kuti malamulo ake akhale olemekezeka.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 22 Koma awa ndi anthu olandidwa zofunkha; onse agwidwa m'maenje, ogwidwa m'ndende; akhala zofunkha popanda wowapulumutsa, ndipo palibe amene akunena kuti, "Abweretseni!"
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 23 Ndani mwa inu adzamvera izi? Ndani adzamve ndikumva mtsogolo? \v 24 Ndani anapereka Yakobo kwa wolanda, ndi Israyeli kwa olanda? Kodi si Yehova, amene tidachimwira Iye, amene adakana kuyenda m'njira zake, ndi kukana kumvera lamulo lake?
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 25 Cifukwa cace anatsanulira pa iwo mkwiyo wace waukuru ndi ciwawa ca nkhondo; Malawi ao anawazinga, koma sanazindikira; chinawawotcha, koma sanachikumbukira.
|
|
@ -496,6 +496,10 @@
|
|||
"42-16",
|
||||
"42-17",
|
||||
"42-18",
|
||||
"42-20",
|
||||
"42-22",
|
||||
"42-23",
|
||||
"42-25",
|
||||
"43-title",
|
||||
"43-01",
|
||||
"43-02",
|
||||
|
|
Loading…
Reference in New Issue