nya-x-nyanja_gen_text_reg/17/15.txt

1 line
248 B
Plaintext

\v 15 Mulungu anakamba kuli Abrahamu kuti, " Mukazi wako Sara, osamuitana futi Sarai. Koma Sarah. \v 16 Nizamudalitsa, ndipo nizakupasa mwana mwamuna muli yeve. Nizamudalitsa, ndipo azankhala mai wamaiko ambiri. Mamfumu abantu azachokela kwa yeve."