nya-x-nyanja_deu_text_reg/19/17.txt

1 line
351 B
Plaintext
Raw Permalink Normal View History

\v 17 Ndiye kuti onse awiri, omwe akukangana, ayenera kuyimirira pamaso pa Yehova, pamaso pa ansembe ndi oweruza omwe amatumikira masiku amenewo. \v 18 Oweruza ayenera kufunsa mwakhama; onani, ngati mboniyo ili mboni yonyenga, ndipo yanenera mbale wake monama, \v 19 mum'chitire monga anafuna kuchitira mbale wake; kuti muchotse choipacho pakati panu.