Thu Apr 18 2024 10:58:07 GMT+0200 (South Africa Standard Time)
This commit is contained in:
parent
3df1fb0334
commit
a6cf40cd39
|
@ -1 +1 @@
|
|||
\v 6 \v 7 Mfumu Rehobiamu anafunsila uphungu ndi akulu amene anaimirira pamaso pa Solomo atate wake ali moyo; Adati: "Mundilangiza bwanji kuti ndiwayankhe anthu awa?" Iwo anamuuza kuti: “Mukawachitira zabwino anthuwa, ndi kuwasangalatsa, ndi kunena mawu abwino kwa iwo, adzakhala atumiki anu nthawi zonse.
|
||||
\v 6 Mfumu Rehobiamu anafunsila uphungu ndi akulu amene anaimirira pamaso pa Solomo atate wake ali moyo; Adati: "Mundilangiza bwanji kuti ndiwayankhe anthu awa?" \v 7 Iwo anamuuza kuti: “Mukawachitira zabwino anthuwa, ndi kuwasangalatsa, ndi kunena mawu abwino kwa iwo, adzakhala atumiki anu nthawi zonse.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 8 Koma Rehobowamu ananyalanyaza uphungu wa akuluwo adamlangiza, nafunsira kwa anyamata anakulira naye, akuima pamaso pake. \v 9 Ndipo iye anati kwa iwo, Mundipangiranji uphungu, kuti tiyankhe anthu amene analankhula nane, kuti, Muchepetse goli limene atate wanu anatisenzetsa?
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 10 \v 11 Anyamata amene anakulira pamodzi ndi Rehobowamu anamuuza kuti: “Ukauze anthu amene anakuuzani kuti Solomo atate wanu analemetsa goli lawo, koma inu mulipeputse. ukawauze kuti, ‘Chala changa chaching’ono n’chachikulu kuposa chiuno cha atate wanga, ndipo tsopano, ngakhale kuti bambo anga anakusenzetsani goli lolemera, + ine ndidzakukwapulani ndi zikoti."
|
|
@ -119,8 +119,8 @@
|
|||
"10-title",
|
||||
"10-01",
|
||||
"10-03",
|
||||
"10-06",
|
||||
"10-08",
|
||||
"10-10",
|
||||
"10-12",
|
||||
"10-15",
|
||||
"10-16",
|
||||
|
|
Loading…
Reference in New Issue