nya-x-nyanja_1ki_text_reg/14/14.txt

1 line
543 B
Plaintext
Raw Blame History

This file contains ambiguous Unicode characters

This file contains Unicode characters that might be confused with other characters. If you think that this is intentional, you can safely ignore this warning. Use the Escape button to reveal them.

\v 14 Komanso Yehova adzautsa mfumu ya Isiraeli imene idzaphe banja la Yerobiamu pa tsiku limenelo. Lero ndi tsiku limenelo, pompano. \v 15 Pakuti Yehova adzaukira Isiraeli ngati bango likugwedezeka mmadzi, ndipo adzazula Isiraeli mdziko labwinoli limene anapereka kwa makolo awo. Iye adzawamwaza kutsidya lina la Mtsinje wa Firate, chifukwa iwo anadzipangira mizati ya Asera ndi kuputa mkwiyo wa Yehova. \v 16 Iye adzasiya Isiraeli chifukwa cha machimo a Yerobowamu, machimo amene anachita, ndiponso amene anachimwitsa nawo Isiraeli.”