Thu Apr 18 2024 16:08:22 GMT+0200 (South Africa Standard Time)
This commit is contained in:
parent
ee32b87d7e
commit
16990402d9
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 27 Mfumu Rehobowamu inapanga zishango zamkuwa m’malo mwake, n’kuzipereka m’manja mwa akuluakulu a asilikali olondera zitseko za nyumba ya mfumu. \v 28 Ndipo kunali kuti, polowa mfumu m'nyumba ya Yehova, odikira ananyamula; Kenako anali kuwabweretsa kunyumba ya alonda.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 29 Nkhani zina zokhudza Rehobowamu ndi zonse zimene anachita, zinalembedwa m’buku la zochitika za m’masiku a mafumu a Yuda. \v 30 Panali nkhondo yokhazikika pakati pa Rehobowamu ndi Yerobiamu. \v 31 Choncho Rehobowamu anagona pamodzi ndi makolo ake ndipo anaikidwa m’manda pamodzi ndi makolo ake mu Mzinda wa Davide. Dzina la amayi ake linali Naama Mamoni. Abiya mwana wake anakhala mfumu m’malo mwake.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
Mutu 15
|
Loading…
Reference in New Issue