nya-x-nyanja_1ki_text_reg/14/23.txt

1 line
297 B
Plaintext
Raw Normal View History

\v 23 Iwo anadzimangiranso malo okwezeka, zipilala zamiyala ndi mizati ya Asera pa zitunda zonse zazitali ndi pansi pa mtengo uliwonse wa masamba obiriwira. \v 24 Mdzikomo munalinso mahule achipembedzo. Anachita zonyansa ngati zimene amitundu amene Yehova anawaingitsa pamaso pa ana a Isiraeli.