\v 23 Iwo anadzimangiranso malo okwezeka, zipilala zamiyala ndi mizati ya Asera pa zitunda zonse zazitali ndi pansi pa mtengo uliwonse wa masamba obiriwira. \v 24 Mā€™dzikomo munalinso mahule achipembedzo. Anachita zonyansa ngati zimene amitundu amene Yehova anawaingitsa pamaso pa ana a Isiraeli.