\v 24 \v 25 \v 26 \v 27 Tsono pambuyo pakumala pa masautso nsiku zomwezo, 'dzuwa lidzaleka kugaka, mwezi udzaleka udzaleka kugaka, nyenyezi zidzagwa kuchokera kudzaulu na mphamvu zomwe ziri kudzaulu zidza gwededzeka; Pomwe adzaona Mwana waMuthu alikubwera m'mitambo na mphamvu zakuwanda na ulemerelo. Tsono iye adzatutumiza achidza gwezeka pabodzi wakusankhuliwa kuchokera ku mphepo zinayi, kuchokera kumalezero ya dziko kukafika mapeto inango.