2020-07-27 15:50:04 +00:00
|
|
|
\v 8 Chakuyamba nitenda Mulungu wangu kuchokela mwaYesu kristu naimwe mwentse, pakuti chikhulupililo chanu chinichemelewa kuchokela pantsi lentse. \v 9 Mulungu ndichapupu changu pomwe ndine mutumiki wafala lamwana wake. \v 10 Ndimbakhala ndichimbakukumbililani kuti ndikhale wakupiyilila nakufuna kwaMulungu pakubwela kwanu.
|