nya-x-nyanja_luk_text_reg/05/36.txt

1 line
287 B
Plaintext

\v 36 Koma Yesu ananena kwaiwo mukanthano. Kulibe anga ng'ambe chinyula muzigao kuchoka kuchanyowani ndiponso kusebenzesa kutungila kuchovala chakudala.Ngati anachita izi, Afunika ang'ambe chanyowani, Ndiponso chigao chanyula kuchoka kuchanyowani, sichinga fanile ndi chinyula chakudala.